Tsiku Laciwili
“Kudzipeleka kwanga panyumba yanu kudzakhala ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga”—Yohane 2:17
M’mawa
-
8:20 Vidiyo ya Nyimbo
-
8:30 Nyimbo Na. 93 ndi Pemphelo
-
8:40 “Kodi Mukufunafuna Ciyani?” (Yohane 1:38)
-
8:50 SEWELO LALIKULA LA M’BAIBO:
Mbili ya Umoyo wa Yesu: Gawo 2
“Uyu Ndiye Mwana Wanga”—Mbali 2 (Yohane 1:19–2:25)
-
9:20 Nyimbo Na. 54 ndi Zilengezo
-
9:30 YOSIYILANA: Tengelani Citsanzo ca Anthu Amene Anali Kukonda Kulambila Koyela!
-
• Yohane M’batizi (Mateyo 11:7-10)
-
• Andireya (Yohane 1:35-42)
-
• Petulo (Luka 5:4-11)
-
• Yohane (Mateyo 20:20, 21)
-
• Yakobo (Maliko 3:17)
-
• Filipi (Yohane 1:43)
-
• Natanayeli (Yohane 1:45-47)
-
-
10:35 UBATIZO: Cifukwa Cake Ubatizo Wanu Ndi Wofunika (Malaki 3:17; Machitidwe 19:4; 1 Akorinto 10:1, 2)
-
11:05 Nyimbo Na. 52 ndi Kupumula
Masana
-
12:35 Vidiyo ya Nyimbo
-
12:45 Nyimbo Na. 36
-
12:50 YOSIYILANA: Gwilitsani Nchito Zimene Mwaphunzilapo pa Cozizwitsa Coyamba ca Yesu
-
• Muzionetsa Cifundo (Agalatiya 6:10; 1 Yohane 3:17)
-
• Khalani Odzicepetsa (Mateyo 6:2-4; 1 Petulo 5:5)
-
• Khalani Owolowa Manja (Deuteronomo 15:7, 8; Luka 6:38)
-
-
13:20 Mmene “Mwanawankhosa wa Mulungu” Amacotsela Ucimo (Yohane 1:29; 3:14-16)
-
13:45 YOSIYILANA: Maulosi Onena za Mesiya Anakwanilitsika!—Gawo 2
-
• Anadzipeleka Kwambili pa Nyumba ya Yehova (Salimo 69:9; Yohane 2:13-17)
-
• Analengeza “Uthenga Wabwino kwa Anthu Ofatsa” (Yesaya 61:1, 2)
-
• Anaonetsa “Kuwala Kwakulu” mu Galileya (Yesaya 9:1, 2)
-
-
14:20 Nyimbo Na. 117 ndi Zilengezo
-
14:30 “Zicotseni Muno Izi!” (Yohane 2:13-16)
-
15:00 “Ndidzamumanganso” (Yohane 2:18-22)
-
15:35 Nyimbo Na. 75 ndi Pemphelo Lothela

