Zokhudza Ife
Kodi Mboni za Yehova Ndani?
Mboni za Yehova ndi cipembedzo cogwilizana pa dziko lonse. Timalambila Yehova amene ndi Mlengi komanso Mulungu wa Mphamvu zonse. (Masalimo 83:18; Cibvumbulutso 4:11) Ndife Akhristu amene timakhulupilila kuti Yesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu komanso Mpulumutsi wathu. (Yohane 3:16; Macitidwe 4:10-12) Zonse zimene timakhulupilila zimacokela m’Baibo. (2 Timoteyo 3:16) Tikupemphani kuti mufufuze zimene timakhulupilila pogwilitsila nchito webusaiti ino komanso Baibo yanu.
Kuti mudziwe zambili zokhudza ife onelelani Vidiyo ya mutu wakuti Mboni za Yehova—Kodi Ndife Anthu Otani?
Ziwelengelo
-
9,205,326—Mboni za Yehova pa dziko lonse
-
119,652—mipingo
-
241—Maiko ndi Madela
-
7,603,182—Maphunzilo a Baibo aulele okambilana amene amatsogozedwa mwezi ulionse
-
20,635,015—Amene anapezeka pa 2025 Cikumbutso ca imfa ya Khristu
Mafunso Ofunsidwa Kawili-kawili
Kodi Mboni za Yehova ndi Akristu?
Dziŵani zimene zimatisiyanitsa ndi zipembedzo zina zimene zimati n’zacikristu.
Maphunzilo a Baibo Aulele
Mbili Yathu
Tilembeleni Kapena Tumani Foni
Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni
Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.
Kapezekemponi pa Misonkhano ya Mboni za Yehova
Fufuzani kumene timakumana komanso mmene timalambilila. Onse ni olandilidwa ndipo sipakhala kuyendetsa mbale ya zopeleka.
Dziŵitsani Mboni za Yehova
Maadilesi ndi manambala a foni a maofesi athu a pa dziko lonse.
Kukaona Malo pa Beteli
Fufuzani kumene mungayende kukaona malo pa Beteli kufupi na kwanu.

