Mbili Yakale komanso Baibo

Baibo ni buku lapadela kwambili tikaganizila zimene zinacitika kuti isungidwe kwa nthawi yaitali, imasulilidwe komanso kufalitsidwa. Zimene akatswili apeza posacedwapa zikupitilizabe kutsimikizila kuti ni yolondola. Kaya muli m’cipembedzo canji, nanunso mungavomeleze kuti Baibo siingalingane na buku ina iliyonse.

NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA

Kaumbidwe ka nchelwa kakale, kaonetsa kuti Baibo ni yolondola

Kodi nchelwa zimene anapeza pa matongwe a Babulo wakale komanso mmene anaziumbila, zionetsa bwanji kuti Baibo ni yolondola?

NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA

Kaumbidwe ka nchelwa kakale, kaonetsa kuti Baibo ni yolondola

Kodi nchelwa zimene anapeza pa matongwe a Babulo wakale komanso mmene anaziumbila, zionetsa bwanji kuti Baibo ni yolondola?