N’ciani Catsopano?
NCHITO YOFALITSA MABUKU
Zithunzi—Ana Amakonda Mavidiyo
Onankoni zimene ana ananena za mavidiyo ochuka ozikidwa pa Baibo akuti ‘Khalani Bwenzi la Yehova,’ a tikadoli ta Kalebe ndi Sofia.
UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO
November–December 2026
NYIMBO ZOPEKEDWA KOYAMBA
Nyumba ya Yehova Ni Malo Acitetezo
Nthawi siinathe, mukhoza kubwelela kwa Yehova.
NYIMBO ZOPEKEDWA KOYAMBA
“Tumakobili Tuŵili”
Yehova amayamikila zonse zimene mumacita, kaya zikhale zazikulu kapena zocepa.
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Mau a m’Baibo—“Lolani Kuti Mtendele wa Khristu Uzilamulila m’Mitima Yanu”
Tingaonetse bwanji kuti tikulola “mtendele wa Khristu” kulamulila m’mitima yathu?
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
September 2026
Magazini ino ili ndi nkhani zophunzila kuyambila November 2–December 6, 2026.
NKHANI ZATSOPANO
Ciunikilo Na. 4 ca Bungwe Lolamulila mu 2026
M’ciunikilo cino, tifotokoza malipoti olimbikitsa a posacedwa, okhudza maulendo aubusa komanso maulendo a oimila likulu amene amacitika ku maofesi a nthambi. Tifotokozanso zocitika zokhudza ufulu wathu wa kulambila ku Norway ndi ku Sweden.

