N’ciani Catsopano?
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Mfundo Zothandiza Powelenga—Mmene Mungapindulile ndi Mavidiyo Athu
Onan’koni malingalilo othandiza kuti muzipindula ndi mavidiyo a pa jw.org.
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Muziyamikila Kuti Ndife Osiyana-siyana
Kodi tingacite ciani kuti tiziona moyenela abale ndi alongo athu, ndi kuyamikila kwambili kusiyana-siyana kwa makhalidwe ao?
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Kodi Asilikali Oteteza Mfumu Anali Kubvala Motani?
Onani mmene gulu la asilikali lochuka limeneli, linali kubvalila ndi mmene linali kudziwikila.
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Mmene Tingakhalile Okhutila Tikakumana ndi Mabvuto a Zacuma
Onani mfundo 4 za m’Baibo zimene zingakuthandizeni kukhala wokhutila pa umoyo wanu.
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
November 2026
Magazini ino ili ndi nkhani zophunzila kuyambila January 4-31, 2027.
KODI ZINANGOCITIKA ZOKHA?
Cule wa Galasi Amene Magazi Ake Saundana—Kodi Zinangocitika Zokha?
Maselo ofiila oculuka a magazi a cule wa galasi amapita ku ciwindi cake, izi zimakhala zoopsya kwambili. N’ciani cimapangitsa culeyu kukhalabe ndi moyo?
GALAMUKA!
Kodi Mungatani ngati Mumakhala Osungulumwa?
Onani cifukwa anthu ambili amakhala osungulumwa, komanso njila zimene zingakuthandizeni kuthana ndi bvutoli, n’colinga coti mudzicitila limodzi zinthu zina ndi ena.
NYIMBO

