Pulogilamu ya Msonkhano wa 2025 wa Mutu Wakuti Kulambila Koyela

Tsiku Loyamba

Pulogilamu ya tsiku loyamba lacokela pa Mateyo 4:10​​—“Yehova Mulungu wako ndi amene uyenela kumulambila.”

Tsiku Laciwili

Pulogilamu ya tsiku laciwili latengedwa pa Yohane 2:17​​—“Kudzipeleka kwanga panyumba yanu kudzakhala ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga.”

Tsiku Lacitatu

Pulogilamu ya tsiku lacitatu yacokela pa Yohane 4:23​​—“[Lambilani] Atate motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi.”

Mawu kwa Osonkhana

malangizo othandiza kwa opezeka pa msonkhano

Mungakondenso Izi

ZOKHUDZA IFE MBONI

Misonkhano Ikuluikulu ya Mboni za Yehova

Anthu onse ndi olandilidwa ku misonkhano yaulele ya pacaka imeneyi.

MISONKHANO IKULUIKULU

Tikukuitanilani ku Msonkhano Wacigawo wa Mboni za Yehova wa 2025 wa Mutu Wakuti “Kulambila Koyela”

Kodi Yesu anaphunzitsa ciyani pa nkhani ya kulambila koona?

MISONKHANO IKULUIKULU

Kadyonkho ka Sewelo Lalikulu la m’Baibo Lakuti: Mbili ya Umoyo wa Yesu: Gawo 2 ndi 3

Tsopano Yesu wakula ndipo wayamba kusonkhanitsa ophunzila ake. Komabe, posacedwa ayamba kutsutsidwa mu utumiki wake.