Kodi zimene Yesu anaphunzitsa n’zothandiza masiku ano?
“Zinthu zonse zimene mumafuna kuti anthu akucitileni, inunso muwacitile zomwezo.”—Mateyo 7:12.
Yesu anaphunzitsanso kuti
-
Tingacepetse nkhawa mwa kupewa kuganizila kwambili za mawa.—Mateyo 6:34.
-
Tiyenela kukhululukila ena.—Mateyo 6:14, 15.
Onelelani vidiyo yakuti, Mbili ya Umoyo wa Yesu pa jw.org.

