Mungacite ciani kuti banja lanu likhale lacimwemwe?

Mungacite Ciani Kuti Banja Lanu Likhale Lacimwemwe?

Cinyanja
Mungacite Ciani Kuti Banja Lanu Likhale Lacimwemwe?
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102024303/afrn/art/1102024303_afrn_sqr_xl.jpg
T-fam masa. 1-2

Mungacite ciani kuti banja lanu likhale lacimwemwe?

Mungacite ciani kuti banja lanu likhale lacimwemwe?

“Aliyense wa inu azikonda mkazi wake ngati mmene amadzikondela yekha komanso mkazi azilemekeza kwambili mwamuna wake.”​Aefeso 5:33.

Baibo imakamba kuti

  • Anthu okwatilana ayenela kukhala okhulupilika kwa wina ndi mnzake.​Mateyo 19:​4-6.

  • Ana amene amalemekeza ndi kumvela makolo ao zinthu zimawayendela bwino.​Aefeso 6:​1-3.

Kuti mudziwe zambili, pitani pa jw.org.