Zokhudza Mboni za Yehova

Mumationa tikugwila nchito yathu yolalikila. Mwina munaŵelengapo za ife pa nyuzi, kapena munamvapo ena akamba za ife. Koma kodi mumazidziŵa bwino motani Mboni za Yehova?

Onaninso: Kodi Mboni za Yehova zimakhulupilila zotani?

Frequently Asked Questions

Kodi Mboni za Yehova ndi Akristu?

Dziŵani zimene zimatisiyanitsa ndi zipembedzo zina zimene zimati n’zacikristu.

Contact Us

Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni

Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.

Kapezekemponi pa Misonkhano ya Mboni za Yehova

Fufuzani kumene timakumana komanso mmene timalambilila. Onse ni olandilidwa ndipo sipakhala kuyendetsa mbale ya zopeleka.

Dziŵitsani Mboni za Yehova

Maadilesi ndi manambala a foni a maofesi athu a pa dziko lonse.

Kukaona Malo pa Beteli

Fufuzani kumene mungayende kukaona malo pa Beteli kufupi na kwanu.