NSANJA YA MLONDA September 2012
NKHANI YA PACIKUTO
Mulungu Amafuna Kuti Akazi Azilemekezedwa
Kodi tiphunzilanji pa khalidwe la Yesu na maganizo ake kwa akazi?
PHUNZILANI M’MAWU A MULUNGU
Kodi pa Tsiku la Ciweluzo Padzacitika Zotani?
Anthu amakhulupilila zosiyana-siyana zokhudza tsiku la ciweluzo. Kodi pali cofunika kuopa? Kodi lidzakwanilitsa ciani?
OŴELENGA AKUFUNSA
Kodi Akazi a Mboni za Yehova Amaphunzitsa Mawu a Mulungu?
Conco kodi amatsatila Mfundo iti ya m’Baibo? Kodi amacita utumiki wotani?
Mungakondenso Izi
ZOKHUDZA IFE MBONI
Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni
Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.

