Kodi Mulungu amakondwela ndi zipembedzo zonse?
“Sikuti aliyense wonena kwa ine kuti, ‘Ambuye, Ambuye,’ adzalowa mu Ufumu wa kumwamba ayi, koma yekhayo wocita cifunilo ca Atate wanga amene ali kumwamba.”—Mateyo 7:21.
Baibo imatiuza kuti
-
Si zipembedzo zonse zimene Mulungu amakondwela nazo.—Mateyo 7:14, 21-23; Maliko 7:6-8.
-
Akhristu oona amalimbikitsa mtendele ndipo amakondana.—Mika 4:3; Yohane 13:35.
Kuti mudziwe zambili, pitani pa jw.org.

