Kodi n’zotheka kukhala ndi moyo kwamuyaya?

Kodi N’zotheka Kukhala ndi Moyo Kwamuyaya?

Cinyanja
Kodi N’zotheka Kukhala ndi Moyo Kwamuyaya?
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102024301/univ/art/1102024301_univ_sqr_xl.jpg
T-ftr masa. 1-2

Kodi n’zotheka kukhala ndi moyo kwamuyaya?

Kodi n’zotheka kukhala ndi moyo kwamuyaya?

“Olungama adzalandila dziko lapansi, ndipo adzakhala mmenemo mpaka kalekale.”​Salimo 37:29.

Baibo imakamba kuti m’tsogolo

  • Matenda onse adzatha.​Yesaya 33:24; 35:​5, 6.

  • Zacilengedwe zimene zaonongedwa zidzakonzedwanso ndipo dziko lidzakhala paradaiso.​Yesaya 35:​1, 2; Chivumbulutso 11:18.

Kuti mudziwe zambili, pitani pa jw.org.