Kodi imfa ndi mapeto a zonse?
“Nthawi ikubwela pamene onse ali m’manda acikumbutso adzamva mau [a Yesu] ndipo adzatuluka.”—Yohane 5:28, 29.
Baibo imatitsimikizila kuti
-
Mulungu adzaukitsa okondedwa athu amene anamwalila.—Machitidwe 24:15.
-
Iye amafunitsitsa kuti adzawaukitse.—Yobu 14:13-15.
Kuti mudziwe zambili, pitani pa jw.org.

