UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO July 2019
Makambilano Acitsanzo
Makambilano otsatizana-tsatizana okamba za cimene cimacititsa mavuto na mmene adzathela.
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Vulani Umunthu Wakale, Muvale Watsopano
Pambuyo pa ubatizo tifunika kupitilizabe kuvula umunthu wakale na kuvala watsopano.
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Pitilizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”
Aliyense wa ife angakwanitse kulimbikitsa ena. Motani?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Wosamvela Malamulo Aonekela
Cinsinsi ca “wosamvela malamulo” cokambidwa pa 2 Atesalonika 2 civumbulidwa.
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kalamilani Nchito Yabwino
Abale obatizika, kuphatikizapo amene akali acicepele, afunika kukalamila. Motani?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Kodi Mungaphunzile Ciani kwa Iwo?
Ngati ndinu mtumiki wothandiza kapena mkulu watsopano, kodi mungaonetse bwanji kuti mumalemekeza aciyambakale? Nanga mungacite ciani kuti muphunzile kwa iwo?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Kudzipeleka kwa Mulungu Kapena ku Cuma
N’cifukwa ciani tingakhale acimwemwe kwambili ngati tadzipeleka kwa Mulungu m’malo mofuna-funa cuma?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Kudzipeleka Kwa Mulungu na Kucita Maseŵela Olimbitsa Thupi
Ni mfundu za m’Baibo ziti zimene zingathandize Akhristu kuona maseŵela olimbitsa thupi moyenelela?

