‘Kulambira Mulungu Motsogoleredwa ndi Mzimu Komanso Coonadi’

‘Kulambira Mulungu Motsogoleredwa ndi Mzimu Komanso Coonadi’

YOHANE 4:24

M’mawa

  • 8:40 Nyimbo Zamalimba

  • 8:50 Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero

  • 9:00 “Atate Akufuna . . . Anthu Ngati Amenewo”

  • 9:15 Yosiyirana: ‘Muzilambira Mulungu Motsogoleredwa ndi Mzimu’

    • • Pamene Mufuna Kumvetsetsa Malangizo a Yehova

    • • Pamene Mukulimbana ndi Zolefula

    • • Pamene Mukuyesetsa Kucita Zambiri

  • 10:05 Nyimbo Na. 88 ndi Zilengezo

  • 10:15 Mmene Timacititsira Kuti Coonadi ‘Cidziwike’

  • 10:35 Ubatizo: Cifukwa Cake Ubatizo Wanu ndi Wofunika

  • 11:05 Nyimbo Na. 51

Masana

  • 12:20 Nyimbo Zamalimba

  • 12:30 Nyimbo Na. 72 ndi Pemphero

  • 12:35 Nkhani ya Anthu Onse: Kodi Tingasiyanitse Bwanji Coyenera ndi Cosayenera?

  • 13:05 Cidule ca Nsanja ya Mlonda

  • 13:35 Nyimbo Na. 56 ndi Zilengezo

  • 13:45 Yosiyirana: ‘Muzilambila Mulungu Motsogoleredwa ndi. . . Coonadi’

    • • M’banja

    • • M’dziko Logawikanali

    • • Mukamakumana ndi Mabvuto a Zacuma

  • 14:30 “Gula Coonadi Ndipo Usacigulitse”

  • 15:00 Nyimbo Na. 29 ndi Pemphero