Acita ulaliki wa mwayi ku South Korea

UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO September 2018

Makambilano Acitsanzo

Makambilano otsatizana-tsatizana a mmene Mulungu amaonela anthu.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Yesu Acita Cozizwitsa Cake Coyamba

Cozizwitsa coyamba ca Yesu citithandiza kudziŵa bwino umunthu wake.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Yesu Alalikila Mayi Wacisamariya

Kuti Yesu acite ulaliki wa mwayi, anayambitsa makambilano mwa kuseŵenzetsa cinthu codziŵika kwa mayiyo.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuyambitsa Makambilano Otsogolela ku Ulaliki

Kodi tinganole bwanji luso lathu loyambitsa makambilano na ŵanthu amene sitiwadziŵa?

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Tsatilani Yesu na Colinga Cabwino

Ophunzila ena anakhumudwa ndipo analeka kutsatila Yesu cifukwa anali na zolinga zadyela.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Sipanawonongeke Ciliconse

Monga Yesu, tingaonetse kuyamikila pa zimene Yehova watipatsa mwa kusakhala wowononga.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Yesu Analemekeza Atate Wake

Cacikulu kwa Yesu cinali kukwanilitsa nchito imene Yehova anam’patsa.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Onetsani Khalidwe la Kudzicepetsa Monga Khristu

Tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu pamene tapatsidwa udindo mu mpingo?