Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

NYIMBO 147

Lonjezo la Moyo Wamuyaya

Lonjezo la Moyo Wamuyaya

(Salimo 37:29)

  1. 1. Mulungu watilonjeza,

    Moyo wokondweletsa.

    Ngati ticita zabwino,

    Tidzaulandila.

    (KOLASI)

    Moyo wamuyaya,

    M’lungu walonjeza,

    Iye sanganame,

    Zidzacitika.

  2. 2. Ana onse a Yehova,

    Adzakhala angwilo.

    Mu Ufumu wa Mulungu,

    Tidzasangalala.

    (KOLASI)

    Moyo wamuyaya,

    M’lungu walonjeza,

    Iye sanganame,

    Zidzacitika.

  3. 3. Posacedwa’pa Mulungu,

    Adzaukitsa anthu.

    Mitundu yonse ya anthu,

    Idzadalitsika.

    (KOLASI)

    Moyo wamuyaya,

    M’lungu walonjeza,

    Iye sanganame,

    Zidzacitika.

(Onaninso Yes. 25:8; Luka 23:43; Yoh. 11:25; Chiv. 21:4.)