NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA February 2019
Magazini ino ili na nkhani zophunzila wiki ya April 8-May 5, 2019
Khalanibe na Mtima Wamphumphu!
Kodi kukhala na mtima wamphumphu kumatanthauzanji? Nanga n’ciani cingatithandize kukhalabe na mtima wamphumphu?
Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Mukondweletse Yehova
Kodi Mose na Yesu anaonetsa bwanji citsanzo cabwino pankhani yokhala wofatsa? Kodi tingapeze madalitso otani ngati tikhala ofatsa?
N’cifukwa Ciani Tiyenela Kuonetsa Kuyamikila?
Kodi tingaphunzile ciani kwa Yehova, Yesu, komanso kwa Msamariya wakhate, pankhani yoonetsa kuyamikila?
Cikondi na Cilungamo M’nthawi ya Aisiraeli
Kodi Cilamulo ca Mose cinaonetsa bwanji mmene Mulungu amaonela cikondi na cilungamo?
MBILI YANGA
Coloŵa Cauzimu Cimene N’nalandila Cinanithandiza Kupita Patsogolo
Ŵelengani nkhani yofotokoza za umoyo wa M’bale Woodworth Mills, amene wakhala akutumikila Yehova mokhulupilika kwa zaka 80.
Kodi mudziŵa?
Kodi masunagoge anayamba bwanji?