N’zotheka Banja Lanu Kukhala Lacimwemwe

Cikwati canu ndi banja lanu lingakhale lacimwemwe ngati mutsatila mfundo za m’Baibulo.

GAWO 1

Dalilani Mulungu Kuti Banja Lanu Likhale Lacimwemwe

Mafunso Aŵili Osavuta Amene Angathandize Banja Lanu Mukawagwilitsila Nchito.

GAWO 2

Khalani Wokhulupilika kwa Wina ndi Mnzake

Kodi kukhala wokhulupilika m’cikwati kumangotanthauza kupewa cigololo?

GAWO 3

Mmene Mungathetsele Mavuto

Kupeza njila yabwino yothetsela mavuto kungacititse kuti banja lanu likhale lolimba komanso lacimwemwe m’malo mokhala losalimba ndi lamavuto.

GAWO 4

Mmene Mungagwilitsile Nchito Ndalama

Kodi kukhala wokhulupilika ndi woona mtima kumathandiza bwanji?

GAWO 5

Mmene Mungakhalile Mwamtendele ndi Acibale Anu

Mungalemekeze makolo anu popanda kusokoneza cikwati canu.

GAWO 6

Mmene Ana Amasinthila Banja

Kodi kubadwa kwa mwana kungalimbitse cikwati canu?

GAWO 7

Mmene Mungaphunzitsile Mwana Wanu

Kulanga kumaphatikizapo zambili osati kungopeleka malamulo ndi cilango coŵaŵa.

GAWO 8

Mavuto Akayamba

Pezani thandizo limene mukufunikila.

GAWO 9

Lambilani Yehova Monga Banja

Mungacite ciani kuti muzisangalala kwambili ndi kulambila kwanu kwa pabanja?