Abulahamu aonetsa kumvela mwa kupita na Isaki ku Moriya

UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO March 2020

Makambilano Acitsanzo

Mpambo wa makambilano onena za Yesu Khristu na nsembe yake.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Mulungu . . . Anamuyesa Abulahamu”

N’cifukwa ciani Yehova anapempha Abulahamu kuti apeleke nsembe mwana wake?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mkazi wa Isaki

Kodi tingaphunzile ciani kwa mtumiki wa Abulahamu pamene tifuna kupanga zosankha zofunika?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kodi Nidzaitanila Ndani?

Ni anthu ena ati amene mungaitanile ku Cikumbutso ca imfa ya Khristu cimene cidzacitika posacedwapa?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Esau Anagulitsa Udindo Wake Monga Woyamba Kubadwa

Ni zinthu zopatulika ziti zimene mufunika kuonetsa kuti mumaziyamikila?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yakobo Analandila Madalitso Omuyenelela

Kodi Yakobo analandila bwanji madalitso ake omuyenelela?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yakobo Akwatila

Kodi mungatani kuti mukhalebe na banja la cimwemwe olo mukumane na mavuto osayembekezela?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kulalikila Anthu Akhungu

Kodi tingatengele bwanji citsanzo ca Yehova pa nkhani yosamalila ndiponso kukonda anthu akhungu m’gawo lathu?