Mose na Aroni akamba na Farao

UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO June 2020

Makambilano Acitsanzo

Mpambo wa makambilano onena za Yesu Khristu na nsembe yake.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yosefe Anakhululukila Abale Ake

Kodi tingaphunzile ciani kwa Yosefe pa nkhani yokhululukila ena?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala

Ngakhale kuti anthu m’dzikoli ali na njala yauzimu, ni kuti kumene tingapeze cakudya cauzimu ca mwana alilenji?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Acikulile Ali na Zambili Zotiphunzitsa

Kodi acikulile amapeleka citsanzo cotani cacikulupililo?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kodi Mungaphunzile Ciani kwa Akhristu Amene ni Aciyambakale?

Kodi mungapindule motani na zinthu zokondweletsa zimene aciyambakale anapeza pa utumiki wawo?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala”

Kodi tanthauzo la dzina la Mulungu limakukhudzani bwanji?

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”

Kodi citsanzo ca Mose cingakulimbikitseni bwanji kuthetsa mantha polalikila?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Moseŵenzetsela Makambilano Acitsanzo

Kodi tiyenela kuseŵenzetsa bwanji makambilano acitsanzo a m’kabuku ka misonkhano pokamba nkhani m’sukulu komanso mu ulaliki ministry?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Mungakwanitse Kulalikila na Kuphunzitsa!

Kodi mungapeze kuti mphamvu na kulimba mtima kuti mukwanitse kulalikila na kuphunzitsa?