2 MBIRI 33–36
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU |Yehova Amaona Munthu Wolapa ndi Mtima Wonse Kukhala Wamtengo Wapatali
MANASE
Yehova analola kuti agwidwe ndi Asuri ndipo anapita naye ku Babulo m’matangadza
ULAMULILO WAKE ASANATENGEDWE KU UKAPOLO
-
Anamangila milungu yonama maguwa ansembe
-
Anapeleka ana ake nsembe
-
Anakhetsa magazi a anthu osalakwa
-
Analimbikitsa anthu onse kucita zamatsenga
ULAMULILO WAKE ATAMASULIDWA
-
Anadzicepetsa kwambili
-
Anapemphela kwa Yehova; ndipo anapeleka nsembe
-
Anacotsa maguwa a nsembe a milungu yonama
-
Analimbikitsa anthu onse kutumikila Yehova
YOSIYA
ULAMULILO WAKE WONSE
-
Anafunafuna Yehova
-
Anayeletsa Yuda ndi Yerusalemu
-
Anakonza nyumba ya Yehova; anapeza buku la Cilamulo ca Yehova