Zatsopano pa JW.ORG
NYIMBO ZATHU
“Kuposa Mpheta Zambiri”
Yehova amaona kuti ndinu ofunika kwambiri ngakhale kuti pena simungadzione choncho. Vidiyo ya nyimboyi ikutikumbutsa kuti ndife ofunika kwambiri kwa Yehova komanso kwa anthu omwe amamukonda.
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
Kodi Mulungu woona ndi ndani?
KHALANI BWENZI LA YEHOVA—ZOCHITA
Yehova Ndi Weniweni
Mungathe kuthandiza ana anu kumudziwa bwino Yehova kudzera mu zinthu zimene analenga.
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
Kodi N’zotheka Kukhala Popanda Zopweteka Zilizonse?
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
Kodi N’zotheka Kukhala ndi Moyo Mpaka Kalekale?
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
Kodi Zipembedzo Zonse Zimasangalatsa Mulungu?
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
Kodi Ufumu wa Mulungu Udzathetsa Bwanji Mavuto Athu?
TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA
Kodi Pali Amene Amamvetsera Mapemphero Athu?
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
Ken Kiuchi: Yehova Wakhala Akundithandiza Kuti Ndikhale Munthu Wabwino
Ken Kiuchi akufotokoza mmene Yehova wamuthandizira kukhala ndi makhalidwe abwino pa nthawi yomwe ankachita upainiya, kutumikira pa Beteli komanso pamene anatumizidwa kuti azikatumikira ku filudi.
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
Muziyesetsa Kuti Muyambirenso Kugwirizana Mwamsanga
Tikamachita zonse zomwe tingathe kuti tithetse kusamvana, timathandiza kuti mumpingo mukhale mtendere komanso timateteza mgwirizano wa abale ndi alongo.
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
Mfundo Yothandiza Pophunzira—Muzikonzekera Ndemanga Zolimbikitsa
Onani mfundo 4 zomwe zingakuthandizeni kuti mukonzekere kukapereka ndemanga zolimbikitsa pamisonkhano.
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
July 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira September 7–October 4, 2026.
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
Mafunso Ochokera kwa Owerenga—June 2026
Kodi Paulo ankanena za mapangano awiri ati pa Agalatiya 4:24?
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
Zinthu Zochititsa Chidwi za M’Baibulo—Maukonde Otchulidwa M’Baibulo
Dziwani zambiri zokhudza maukonde otchulidwa m’Baibulo amene asodzi ankagwiritsa ntchito.
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
Ndakhala Ndikutumikira Yehova ku Cuba kwa Zaka Pafupifupi 70
Gustavo Joseph akufotokoza mmene zinthu zinalili pa moyo wawo pa nthawi imene ankachita utumiki woyang’anira dera, ankalera ana komanso kutumikira pa Beteli.
NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA
June 2026
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira August 10–September 6, 2026.
MFUNDO ZA NSANJA YA OLONDA YOPHUNZIRA

