Zatsopano pa JW.ORG

2026-08-04

NYIMBO ZATHU

“Kuposa Mpheta Zambiri”

Yehova amaona kuti ndinu ofunika kwambiri ngakhale kuti pena simungadzione choncho. Vidiyo ya nyimboyi ikutikumbutsa kuti ndife ofunika kwambiri kwa Yehova komanso kwa anthu omwe amamukonda.

2026-07-30

TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA

Kodi Mulungu woona ndi ndani?

2026-07-30

KHALANI BWENZI LA YEHOVA​—ZOCHITA

Yehova Ndi Weniweni

Mungathe kuthandiza ana anu kumudziwa bwino Yehova kudzera mu zinthu zimene analenga.

2026-07-29

TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA

Kodi N’zotheka Kukhala ndi Moyo Mpaka Kalekale?

2026-07-29

TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA

Kodi Zipembedzo Zonse Zimasangalatsa Mulungu?

2026-07-29

TIMAPEPALA NDI ZOITANIRA

Kodi Pali Amene Amamvetsera Mapemphero Athu?

2026-07-27

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

Ken Kiuchi: Yehova Wakhala Akundithandiza Kuti Ndikhale Munthu Wabwino

Ken Kiuchi akufotokoza mmene Yehova wamuthandizira kukhala ndi makhalidwe abwino pa nthawi yomwe ankachita upainiya, kutumikira pa Beteli komanso pamene anatumizidwa kuti azikatumikira ku filudi.

2026-07-27

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

Muziyesetsa Kuti Muyambirenso Kugwirizana Mwamsanga

Tikamachita zonse zomwe tingathe kuti tithetse kusamvana, timathandiza kuti mumpingo mukhale mtendere komanso timateteza mgwirizano wa abale ndi alongo.

2026-07-27

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

Mfundo Yothandiza Pophunzira​​—⁠Muzikonzekera Ndemanga Zolimbikitsa

Onani mfundo 4 zomwe zingakuthandizeni kuti mukonzekere kukapereka ndemanga zolimbikitsa pamisonkhano.

2026-07-27

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

July 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira September 7–​October 4, 2026.

2026-07-14

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

Mafunso Ochokera kwa Owerenga​​—⁠June 2026

Kodi Paulo ankanena za mapangano awiri ati pa Agalatiya 4:24?

2026-07-14

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

Zinthu Zochititsa Chidwi za M’Baibulo​​—⁠Maukonde Otchulidwa M’Baibulo

Dziwani zambiri zokhudza maukonde otchulidwa m’Baibulo amene asodzi ankagwiritsa ntchito.

2026-07-14

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

Ndakhala Ndikutumikira Yehova ku Cuba kwa Zaka Pafupifupi 70

Gustavo Joseph akufotokoza mmene zinthu zinalili pa moyo wawo pa nthawi imene ankachita utumiki woyang’anira dera, ankalera ana komanso kutumikira pa Beteli.

2026-07-14

NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA

June 2026

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira August 10–​September 6, 2026.

2026-07-14

MFUNDO ZA NSANJA YA OLONDA YOPHUNZIRA

October 2026