2026 Convention Program

KOPERANI

Watchtower LAIBULALE YA PA INTANET™

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOKHUDZA IFEYO

Misonkhano Yapachaka ya Mboni za Yehova

Aliyense ndi wolandiridwa ku misonkhanoyi ndipo ndi yaulere.

MISONKHANO IKULUIKULU

Mukuitanidwa Kumsonkhano wa Mboni za Yehova wa 2026 Wakuti “Chimwemwe Chosatha”

Bwerani kuti mudzakhale nafe Pamsonkhano wa 2026 wakuti “Chimwemwe Chosatha” kuti mudzaphunzire mmene kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Mlengi, kungakuthandizireni kupeza chimwemwe chosatha.

MISONKHANO IKULUIKULU

Zimene Zili Muvidiyo Yakuti: Uthenga Wabwino wa Yesu, Gawo 4, 5 ndi 6

N’chifukwa chiyani anthu ankabwera kwa Yesu? Nanga zimene ankalankhula zitasiyana ndi zimene atsogoleri achipembedzo ankakhulupirira, chinachitika n’chiyani?