Pulogalamu ya Msonkhano wa 2023 wakuti “Khalani Oleza Mtima”
Lachisanu
Pulogalamu ya Lachisanu yachokera palemba la 1 Akorinto 13:4—“Chikondi n’choleza mtima.”
Loweruka
Pulogalamu ya Loweruka ikuchokera palemba la 1 Atesalonika 5:14—“Khalani oleza mtima kwa onse.”
Lamlungu
Pulogalamu ya Lamlungu yachokera pa lemba la Yesaya 30:18—‘Yehova akuyembekezera moleza mtima kuti akukomereni mtima.’
Mawu kwa Osonkhana
Mfundo zothandiza kwa omwe asonkhana.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZOKHUDZA IFEYO
Misonkhano Yapachaka ya Mboni za Yehova
Aliyense ndi wolandiridwa ku misonkhanoyi ndipo ndi yaulere.

