Zokhudza Mboni za Yehova

Gawo lino likuthandizani ngati mukufuna kulankhula nafe, kufika pamisonkhano yathu, kupempha munthu woti aziphunzira nanu Baibulo kapenanso ngati mukungofuna kudziwa zambiri zokhudza ife. Tikukupemphaninso kuti mubwere kudzaona malo kumaofesi athu kuti mudziwe mmene ntchito yathu imayendera.

Onaninso: Kodi a Mboni za Yehova Amakhulupirira Zotani?

Tipezeni

Pemphani Kuti Tidzakuyendereni

Mutha kukhala ndi mwayi wokambirana nkhani inayake ya m’Baibulo kapena kudziwa zambiri zokhudza Mboni za Yehova.

Fikani Pamsonkhano

Dziwani zambiri zokhudza misonkhano yathu. Pezani malo apafupi amene kumachitikira misonkhano yathu.