KUKHULUPILILA MULUNGU

Kukhala na Makhalidwe Abwino

Cinyanja
Kukhala na Makhalidwe Abwino
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1011580/univ/art/1011580_univ_sqr_xl.jpg

Kukhala na Makhalidwe Abwino

Njila Yopezela Cimwemwe​—Kukhutila Komanso Kupatsa

Ambili amaganiza kuti munthu amakhala wacimwemwe akapeza cuma cambili. Kodi kukhala na ndalama komanso katundu wambili kumabweletsa cimwemwe cokhalitsa? Kodi zocitika zimaonetsa ciani?

Kupatsa Kumapindulitsa

Kupatsa kumapindulitsa inu ndi ena. Kumalimbikitsa mgwilizano na ubwenzi. Mungacite ciani kuti muzipeleka mokondwela?

Njila Yopezela Cimwemwe​—Cikondi

Kuonetsana cikondi n’kofunika kwambili kuti munthu akhale wacimwemwe.

Tsankho​—Onetsani Cikondi

Kuonetsa cikondi kumathetsa tsankho. Ganizilani zimene mungacite.

Tsankho—Onetsani Cifundo

Kodi kusoŵa cifundo kungakhale cizindikilo ca ciani?

Kufatsa​—Kumaonetsa Nzelu

Si capafupi kukhalabe wofatsa tikacitilidwa zinthu mopanda cilungamo, koma Baibo imalimbikitsa Akhiristu kukhala ofatsa. N’ciani cingakuthandizeni kukhala na khalidwe laumulungu limeneli?

Njila Yopezela Cimwemwe​—Kukhululuka

Umoyo wokhala wokhumudwa na kusunga cakukhosi, si umoyo wacimwemwe ndipo umaononga thanzi.