Phunzilani kwa Mabwenzi a Yehova—Zocita

Gwilitsani nchito zocita izi kupanga zithunzi za m’mavidiyo akuti Phunzilani kwa Mabwenzi a Yehova, ndipo kambilanani maphunzilo ofunika ndi ana anu.

Mefiboseti

Mungacite ciani kuti mukhalebe acimwemwe mukacitilidwa zopanda cilungamo monga anacitila Mefiboseti?

Yosefe

Mungaphunzile ciani kwa Yosefe amene anali mnzake wa Yehova?

Yoswa ndi Kalebe

Kodi mungaphunzile ciani kwa Yoswa ndi Kalebe amene anali mabwenzi a Yehova?

Abigayeli

Mungaphunzile ciyani kwa Abigayeli amene anali bwenzi la Yehova?

Debora

Kodi mungaphunzile kwa Debora amene anali bwenzi la Yehova

Pepani, palibe mawu olingana amene mwasankha.