ZIPHUNZITSO ZOFUNIKA ZA M’BAIBO

Dziko Linasintha Kuyambila mu 1914

Cinyanja
Dziko Linasintha Kuyambila mu 1914
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102020419/univ/art/1102020419_univ_sqr_xl.jpg
ebtv

Dziko Linasintha Kuyambila mu 1914

Dziko Linasintha Kuyambila mu 1914

Baibo inafotokozelatu zocitika komanso makhalidwe a anthu amene adzaonetsa kuti tili ‘m’masiku otsiliza.’ (2 Timoteyo 3:1) Onani mmene zizindikilo za masiku otsiliza zimenezi zaonekela bwino kuyambila mu 1914.