Cinyanja
Wiki Yomaliza ya Yesu Padziko Lapansi (Mbali 1)
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1001061100/univ/wpub/1001061100_univ_sqr_xl.jpg
nwt masa. 570-571

B12

Wiki Yomaliza ya Yesu Padziko Lapansi (Mbali 1)

Yerusalemu ndi Madela Ozungulila

  1. Kacisi

  2. Munda wa Getsemani (?)

  3. Nyumba ya Bwanamkubwa

  4. Nyumba ya Kayafa (?)

  5. Nyumba ya Herode Antipa (?)

  6. Dziwe la Betesida

  7. Dziwe la Siloamu

  8. Holo ya Sanihedirini (?)

  9. Gologota (?)

  10. Munda wa Magazi (?)

    Zocitika za pa:  Nisani 8 |  Nisani 9 |  Nisani 10 |  Nisani 11

 Nisani 8 (Sabata)

DZUWA LITALOWA (Masiku a Ayuda anali kuyamba ndi kutha dzuwa likalowa)

  • Afika ku Betaniya kutatsala masiku 6 kuti Pasika acitike

M’MAWA

DZUWA LITALOWA

 Nisani 9

DZUWA LITALOWA

  • Akudya ndi Simoni wakhate

  • Mariya adzoza Yesu ndi nado

  • Ayuda apita kukaona Yesu komanso Lazaro

M’MAWA

  • Alowa mu Yerusalemu mwaulemelelo

  • Aphunzitsa m’kacisi

DZUWA LITALOWA

 Nisani 10

DZUWA LITALOWA

  • Agona ku Betaniya

M’MAWA

  • Alawilila kupita ku Yerusalemu

  • Ayeletsa kacisi

  • Yehova alankhula kucokela kumwamba

DZUWA LITALOWA

 Nisani 11

DZUWA LITALOWA

M’MAWA

  • Asewenzetsa mafanizo pophunzitsa m’kacisi

  • Adzudzula Afarisi

  • Aona pamene mkazi wamasiye akucita copeleka

  • Ali pa Phili la Maolivi ndipo akambilatu za kuonongedwa kwa Yerusalemu, komanso apeleka cizindikilo ca kukhalapo kwake

DZUWA LITALOWA