A7-A
Zocitika Zikulu-zikulu mu Umoyo wa Yesu Ali Padziko Lapansi—Zimene Zinacitika Yesu Asanayambe Utumiki Wake
Zocitika za m’mabuku a Uthenga Wabwino Zandandalikidwa Motsatila Nthawi Imene Zinacitika
Machati otsatila ali ndi mapu oonetsa mmene Yesu anayendela komanso malo kumene analalikilako. Zizindikilo za ngati mivi pa mapu, sizikuonetsa njila zenizeni zimene anadutsa, koma zikuonetsa madela kumene anafikako. Cizindikilo ca “c.” citanthauza “ca m’ma.”
Zimene Zinacitika Yesu Asanayambe Utumiki Wake
|
NTHAWI |
MALO |
COCITIKA |
MATEYO |
MALIKO |
LUKA |
YOHANE |
|---|---|---|---|---|---|---|
|
3 B.C.E. |
Yerusalemu, m’kacisi |
Mngelo Gabirieli auzilatu Zekariya za kubadwa kwa Yohane M’batizi |
||||
|
c. 2 B.C.E. |
Nazareti; Yudeya |
Mngelo Gabirieli auzilatu Mariya za kubadwa kwa Yesu; Mariya apita kukaona Elizabeti |
||||
|
2 B.C.E. |
Dela lamapili la Yudeya |
Kubadwa kwa Yohane M’batizi komanso kupatsidwa dzina; Zekariya alosela; Yohane apita ku cipululu |
||||
|
2 B.C.E., c. Oct. 1 |
Betelehemu |
Yesu abadwa; “Mauyo anakhala munthu” |
||||
|
Kufupi ndi Betelehemu; Betelehemu |
Mngelo alengeza uthenga wabwino kwa abusa; angelo atamanda Mulungu; abusa apita kukaona mwana |
|||||
|
Betelehemu; Yerusalemu |
Yesu adulidwa (pa tsiku la 8); makolo apita naye ku kacisi (pambuyo pa masiku 40) |
|||||
|
1 B.C.E. kapena 1 C.E. |
Yerusalemu; Betelehemu; Iguputo; Nazareti |
Okhulupilila nyenyezi apita kukaona Yesu; banja lithawila ku Iguputo; Herode akupha ana aamuna; banja libwelako ku Iguputo ndipo likhazikika ku Nazareti |
||||
|
12 C.E., Pasika |
Yerusalemu |
Yesu ali ndi zaka 12 ndipo ali mu kacisi kufunsa mafunso aphunzitsi |
||||
|
Nazareti |
Abwelela ku Nazareti; apitiliza kumvela makolo ake; aphunzila nchito yaukalipentala; Mariya abeleka ana ena anai aamuna komanso aakazi (Mt 13:55, 56; Mko 6:3) |
|||||
|
29, cakumayambililo kwa caka |
Cipululu, Mtsinje wa Yorodano |
Yohane M’batizi ayamba utumiki wake |

