A7-E
Zocitika Zikulu-zikulu mu Umoyo wa Yesu Ali Padziko Lapansi—Utumiki wa Yesu mu Galileya (Mbali 3) Komanso mu Yudeya
|
NTHAWI |
MALO |
COCITIKA |
MATEYO |
MALIKO |
LUKA |
YOHANE |
|---|---|---|---|---|---|---|
|
32, pambuyo pa Pasika |
Nyanja ya Galileya; Betsaida |
Akwela bwato kupita ku Betsaida, Yesu awacenjeza za cofufumitsa ca Afarisi; acilitsa munthu wakhungu |
||||
|
Kaisareya wa ku Filipi |
Makiyi a Ufumu; akambilatu za imfa yake ndi kuukitsidwa |
|||||
|
Mwina pa Phili la Herimoni |
Kusandulika; Yehova alankhula |
|||||
|
Kaisareya wa ku Filipi |
Acilitsa mnyamata wogwidwa ndi ciwanda |
|||||
|
Galileya |
Akambilatunso za imfa yake |
|||||
|
Kaperenao |
Akhoma msonkho ndi ndalama imene apeza mkamwa mwa nsomba |
|||||
|
Amene ali wamkulu kwambili mu Ufumu; fanizo la nkhosa yosocela komanso la kapolo wosakhululuka |
||||||
|
Galileya-Samariya |
Apita ku Yerusalemu, auza ophunzila kuika patsogolo Ufumu |
Utumiki Womaliza Umene Yesu Anacita ku Yudeya
|
NTHAWI |
MALO |
COCITIKA |
MATEYO |
MALIKO |
LUKA |
YOHANE |
|---|---|---|---|---|---|---|
|
32, Cikondwelelo ca Misasa (kapena kuti ca Mahema) |
Yerusalemu |
Aphunzitsa pa Cikondwelelo; asilikali atumidwa kukagwila Yesu |
||||
|
Akamba mau akuti “Ine ndine kuwala kwa dziko”; acilitsa munthu yemwe anabadwa wakhungu |
||||||
|
Mwina ku Yudeya |
Atuma ophunzila 70 ndipo iwo abwelako ali acimwemwe |
|||||
|
Yudeya; Betaniya |
Fanizo la Msamariya wacifundo; apita kukaona Mariya ndi Marita kunyumba kwao |
|||||
|
Mwina ku Yudeya |
Pemphelo lacitsanzo; fanizo lokhudza kulimbikila ndi kupemphela |
|||||
|
Atulutsa ziwanda ndi cala ca Mulungu; apelekanso cizindikilo ca Yona |
||||||
|
Akudya ndi Mfarisi; adzudzula cinyengo ca Afarisi |
||||||
|
Mafanizo: munthu wolemela wopanda nzelu komanso mtumiki wokhulupilika |
||||||
|
Acilitsa mzimai wopindika msana pa Sabata; fanizo la kanjele ka mpilu komanso la zofufumitsa |
||||||
|
32, Cikondwelelo Copeleka Kacisi kwa Mulungu |
Yerusalemu |
Fanizo la m’busa wabwino; Ayuda afuna kumuponya miyala; acoka ndipo apita ku Betaniya wa kutsidya la Yorodano |

