Cinyanja
Zocitika Zikulu-zikulu mu Umoyo wa Yesu Ali Padziko Lapansi—Utumiki Waukulu Umene Yesu Anacita mu Galileya (Mbali 2)
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1001061100/univ/wpub/1001061100_univ_sqr_xl.jpg
nwt masa. 554-555

A7-D

Zocitika Zikulu-zikulu mu Umoyo wa Yesu Ali Padziko Lapansi—Utumiki Waukulu Umene Yesu Anacita mu Galileya (Mbali 2)

NTHAWI

MALO

COCITIKA

MATEYO

MALIKO

LUKA

YOHANE

31 kapena 32

Dela la Kaperenao

Yesu afotokoza mafanizo a Ufumu

13:1-53

4:1-34

8:4-18

 

Nyanja ya Galileya

Akhalitsa bata namondwe pomwe ali m’bwato

8:18, 23-27

4:35-41

8:22-25

 

Dela la Dadara

Atumiza ziwanda m’nkhumba

8:28-34

5:1-20

8:26-39

 

Mwina ku Kaperenao

Acilitsa mzimai amene anali ndi matenda otaya magazi; aukitsa mwana wamkazi wa Yairo

9:18-26

5:21-43

8:40-56

 

Kaperenao (?)

Acilitsa munthu wakhungu komanso munthu wosalankhula

9:27-34

     

Nazareti

Akanidwanso mumzinda wakwao

13:54-58

6:1-5

   

Galileya

Ulendo wacitatu wa ku Galileya; atumiza atumwi kukalalikila

9:35–11:1

6:6-13

9:1-6

 

Tiberiyo

Herode adula mutu Yohane M’batizi; Herode athedwa nzelu atamva za Yesu

14:1-12

6:14-29

9:7-9

 

32, Pasika atayandikila (Yoh 6:4)

Kaperenao (?); Kumpoto cakum’mawa kwa Nyanja ya Galileya

Atumwi abwelako kokalalikila; Yesu adyetsa amuna 5,000

14:13-21

6:30-44

9:10-17

6:1-13

Kumpoto cakum’mawa kwa Nyanja ya Galileya; Genesareti

Ayesa kulonga Yesu ufumu; ayenda pamadzi; acilitsa anthu ambili

14:22-36

6:45-56

 

6:14-21

Kaperenao

Yesu akamba kuti iye ndi “cakudya copatsa moyo”; ambili asiya kumutsatila

     

6:22-71

32, Pambuyo pa Pasika

Mwina ku Kaperenao

Awadzudzula cifukwa ca miyambo

15:1-20

7:1-23

 

7:1

Foinike; Dekapole

Acilitsa mwana wamkazi wa mai wacisirofoinike; adyetsa amuna 4,000

15:21-38

7:24–8:9

   

Magadani

Apeleka cizindikilo ca Yona

15:39–16:4

8:10-12