A7-B
Zocitika Zikulu-zikulu mu Umoyo wa Yesu Ali Padziko Lapansi—Ciyambi ca Utumiki wa Yesu
|
NTHAWI |
MALO |
COCITIKA |
MATEYO |
MALIKO |
LUKA |
YOHANE |
|---|---|---|---|---|---|---|
|
29, cakumapeto kwa caka |
Mtsinje wa Yorodano, kapena kufupi ndi Betaniya wa kutsidya kwa Yorodano |
Ubatizo ndi kudzozedwa kwa Yesu; Yehova amulengeza kuti ndi Mwana wake komanso kuti amakondwela naye |
||||
|
Cipululu ca Yudeya |
Ayesedwa ndi Mdyelekezi |
|||||
|
Betaniya wa kutsidya lina la Yorodano |
Yohane M’batizi akamba kuti Yesu ndi Mwanawankhosa wa Mulungu; ophunzila oyambilila atsatila Yesu |
|||||
|
Kana wa ku Galileya; Kaperenao |
Cozizwitsa coyamba, asandutsa madzi kukhala vinyo; apita ku Kaperenao |
|||||
|
30, Pasika |
Yerusalemu |
Ayeletsa kacisi |
||||
|
Akambilana ndi Nikodemo |
||||||
|
Yudeya; Ainoni |
Apita kumidzi ya ku Yudeya, ophunzila ake abatiza anthu; umboni womaliza wa Yohane wokhudza Yesu |
|||||
|
Tiberiyo; Yudeya |
Yohane aikidwa m’ndende; Yesu acoka apita ku Galileya |
|||||
|
Sukari, ku Samariya |
Pa ulendo wa ku Galileya, aphunzitsa Asamariya |
Cipululu ca Yudeya

