Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

WATCHTOWER LIBRARY

Ikani Watchtower Library

Ikani Watchtower Library

Tsatirani malangizo awa kuti mupange dawunilodi komanso kuika Watchtower Library:

  1. 1. Dinani batani la Dawunilodi patsamba lino.

  2. 2. Sankhani chinenero, kenako batani la Dawunilodi kuti mupeze failo ya Watchtower Library .exe.

  3. 3. Dinani kawiri failo yomwe mwadawunilodayo, kenako tsatirani malangizo omwe ali pasikirini kuti muike Watchtower Library.

  4. 4. Popeza kuti mukaika Watchtower Library koyamba simukhala zinthu za mulaibulaleyi, tsatirani izi kuti mupange dawunilodi zinthuzi:

    1. a. Tsegulani Watchtower Library.

    2. b. Pitani pa Help, kenako sankhani Check for Updates kuti mudawunilode zinthu mulaibulaleyi.

    Njira ina, mungatsatire malangizo omwe ali pa “Update Watchtower Library kuti mupange dawunilodi ndiponso kuika failo yochitira update.