Pitani ku nkhani yake

ZITHUNZI

Davide Analimba Mtima Ngakhale Kuti Anali ndi Zida Zochepa

Fananitsani anthu otchulidwa m’Baibulo ndi zinthu zokhudza anthuwo zomwe zili m’nkhani ya Davide ndi Goliyati. Kenako mukambirane zimene zinathandiza Davide kuti akhale wolimba mtima.