Chichewa
Zithunzi Zofotokoza Nkhani za M’Baibulo
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1011257/univ/art/1011257_univ_sqr_xl.jpg

Zithunzi Zofotokoza Nkhani za M’Baibulo

Yerekezerani kuti mukuona zimene mukuwerenga pa zithunzi zofotokoza nkhani za m’Baibulozi zikuchitikadi. Kenako yankhani mafunso amene ali kumapeto kwa nkhaniyi monga banja n’kukambirana zimene mukuphunzira.