Thandizani Kalebe Kukonza M’nyumba
Pangani dawunilodi tsambali, ndipo thandizani Kalebe kuti apeze zidole zake 5. Kalebe akufuna kumvera mayi ake pochotsa zidole zake m’nyumbamo.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Uzikhala Waukhondo
Yehova amaika chilichonse pamalo oyenera. Onani zimene nanunso mungachite kuti muzikhala aukhondo