Kunyumba ndi Nyumba
Yehova amatipatsa zinthu zosiyanasiyana zotithandiza polalikira. Kodi ndi zinthu ziti zomwe ungagwiritse ntchito? Tiyeni tione.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
KHALANI BWENZI LA YEHOVA
Nyimbo 83—“Kunyumba ndi Nyumba” (Nyimbo 83)
Inunso mungathandize nawo kulengeza za uthenga wa Ufumu!