Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Turkmenistan

 

2016-03-02

TURKMENISTAN

Dziko la Turkmenistan Linagamula Kuti a Bahram Hemdemov Akhale M’ndende Zaka 4 Chifukwa cha Chipembedzo

Apolisi anaphwanya malamulo posokoneza msonkhano umene unkachitikira m’nyumba ya a Bahram Hemdemov. Akuluakulu a makhoti anachitanso zinthu mopanda chilungamo.

2014-12-03

TURKMENISTAN

Dziko la Turkmenistan Latulutsa M’ndende a Mboni Omwe Anamangidwa Chifukwa Chotsatira Zimene Amakhulupirira

Pa October 22, 2014, Pulezidenti Berdimuhamedov analamula kuti a Mboni za Yehova 8 omwe anamangidwa chifukwa chotsatira zimene amakhulupirira atulutsidwe m’ndende.

2014-10-22

TURKMENISTAN

Mayi Wina Watulutsidwa Kundende M’dziko la Turkmenistan

Bibi Rahmanova anatulutsidwa m’ndende mwadzidzidzi pa September 2, 2014. Ngakhale kuti mayiko ndi mabungwe ena anadandaula za nkhaniyi, oweruza sanathetse mlanduwu.

2014-10-10

TURKMENISTAN

Mayi wa Mwana Wazaka 4 ku Turkmenistan Amuweruza Mopanda Chilungamo Kuti Akakhale Kundende

Dziko la Turkmenistan limakonda kuchitira nkhanza a Mboni za Yehova komanso kuwaphwanyira ufulu wachibadwidwe. Mayi Bibi Rahmanova ndi banja lawo akuchitiridwa zopanda chilungamo ndi akuluakulu a boma a ku Dashoguz.