Kuona Malo ku Beteli
Tikukuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi omwenso amadziwika kuti Beteli. Ku maofesi athu ena kulinso malo achionetsero omwe mukhoza kuona nokha popanda wokutsogolerani.
Cameroon
Les Témoins de Jéhovah du Cameroun
Ancienne Route SONEL
Bonamikano, Bonabéri,
DOUALA
CAMEROON
+237 3339-0250
+237 3339-2101
Kuona Malo
Lachitatu ndi Lachisanu
2:00 p.m. mpaka 4:30 p.m.
Nthawi yonse: Mphindi 30
Zimene Timachita
Timayang’anira ntchito imene anthu a Mboni za Yehova oposa 40,000 akugwira m’mayiko a Cameroon, Gabon ndi Equatorial Guinea. Timatumiza mabuku m’mayiko asanu a ku Africa.

