Kodi Zopereka Zanu Zimagwiritsidwa Ntchito Bwanji?
Ntchito ya Mboni za Yehova imayendetsedwa ndi zopereka zaufulu. Werengani kuti mudziwe mmene zoperekazi zimagwiritsidwira ntchito pothandiza anthu padziko lonse.
Kusamalira Nyumba za Ufumu
Padziko lonse tili ndi Nyumba za Ufumu zoposa 60,000. Kodi timasamalira bwanji nyumbazi?
Kuchita Zinthu Zothandiza Abale Athu Komanso Zosawononga Chilengedwe
Onani mmene tikugwiritsira ntchito zinthu zosawononga chilengedwe komanso mmene tachepetsera kugwiritsira ntchito zinthu monga malasha, mafuta komanso gasi.
Misonkhano Imene Anthu ‘Amamva ndi Kuona’
Onani zimene zimachitika kuti tizitha kumvetsera nkhani komanso kuonera mavidiyo pamisonkhano yathu.
Kuteteza Anthu pa Nyumba za Ufumu Panthawi ya COVID-19
Tinayambiranso kusonkhana pamasom’pamaso pa 1 April 2022. Werengani nkhaniyi kuti muone zimene zinachitika kuti abale ndi alongo akhale otetezeka akasonkhana m’Nyumba za Ufumu.
Sitinaiwale Abale ndi Alongo Athu Powathandiza Pangozi Zogwa Mwadzidzidzi mu 2021
M’chaka cha 2021, m’mayiko ena anthu ankafunika kuthandizidwa chifukwa cha mliri wa COVID-19 komanso ngozi zikuluzikulu zam’chilengedwe.
Mabuku a Zilembo za Anthu Osaona Akuthandiza Kwambiri
Timapanga mabuku a zilembo za anthu osaona komanso kuphunzitsa anthu kuwerenga mabukuwa.
Laibulale Yokwanira M’dzanja Limodzi
Pulogalamu ya JW Library yafotokozedwa kuti “ndi yamtengo wapatali kwambiri.” Onani zimene zimafunika kuti izikonzedwa komanso kusinthidwa.
Kuonera Kapena Kumvetsera Msonkhano
Msonkhano wachigawo wa chaka cha 2020 unaikidwa pa intaneti, koma anthu ambiri ku Malawi ndi ku Mozambique sangakwanitse kugwiritsa ntchito intaneti. Ndiye kodi anatha bwanji kumvetsera msonkhanowu?
Kupereka Chithandizo Padziko Lonse pa Nthawi ya Mliri
Zimene tachita popereka chithandizo pa nthawi ya mliri wa COVID-19 zadabwitsa a Mboni komanso amene si Mboni.
Amishonale Amapita “Kumalekezero a Dziko Lapansi”
Kuli amishonale oposa 3,000 omwe akutumikira m’mayiko osiyanasiyana padziko lonse lapansi. Kodi amasamaliridwa bwanji?
Anateteza Ufulu wa Kulambira wa Anthu Akumidzi
Pamene anthu otsutsa anaphwanyira a Mboni za Yehova ufulu wawo wa kulambira, abale athu anawathandiza mwamsanga.
Tchanelo cha JW Setilaiti Chimaoneka Kumene Kulibe Intaneti
Kodi abale a ku Africa amatani kuti aonere JW Broadcasting ngati alibe intaneti?
Maofesi a Omasulira Mabuku Omwe Akuthandiza Anthu Mamiliyoni
Dziwani mmene malo amene omasulira amagwirira ntchito yawo amakhudzira zimene akumasulira.
Kuthandiza Anthu Amene Akhudzidwa Ndi Ngozi Zadzidzidzi
M’chaka chautumiki cha 2020, abale ndi alongo ambiri anakhudzidwa ndi mliri komanso ngozi zam’chilengedwe. Kodi tinawathandiza bwanji?
Ntchito Yomasulira Buku Lofunika Kwambiri
Pali zinthu zambiri zomwe zimafunikira kuti Baibulo la Dziko Latsopano limasuliridwe komanso kusindikizidwa.
Mmene Sukulu ya Giliyadi Imathandizira Padziko Lonse
Sukulu yofunika kwambiri imachitikira ku New York, koma ophunzira amachokera m’mayiko osiyanasiyana padziko lonse. Ndiye kodi ophunzirawa amayenda bwanji kuti akafike kusukuluyi?
Zimene Ena Ali Nazo Zimathandizira pa Zimene Ena Akusowa
Kodi mayiko amene amapeza ndalama zochepa amathandizidwa bwanji kuti ntchito yathu iziyenda bwino?
Kachipangizo Kothandiza Kwambiri
A Mboni za Yehova ambiri akutha kupanga dawunilodi mabuku ndi mavidiyo athu popanda kugwiritsa ntchito intaneti.
Ntchito Yokonza Mavidiyo a Msonkhano Wachigawo wa 2020 Wakuti “Kondwerani Nthawi Zonse”
Kodi pamafunikanso zinthu ziti pokonza mavidiyo a misonkhano yathu yachigawo?
Ntchito Yomasulira Msonkhano Wachigawo wa 2020 Wakuti ‘Kondwerani Nthawi Zonse.’
Kodi n’chiyani chinathandiza kuti nkhani, masewero komanso nyimbo zimasuliridwe mofulumira kwambiri, m’zinenero zoposa 500?
KUFALITSA CHAKUDYA CHAUZIMU
Ntchito Yomasulira Buku Lofunika Kwambiri
Pali zinthu zambiri zomwe zimafunikira kuti Baibulo la Dziko Latsopano limasuliridwe komanso kusindikizidwa.
Mabuku a Zilembo za Anthu Osaona Akuthandiza Kwambiri
Timapanga mabuku a zilembo za anthu osaona komanso kuphunzitsa anthu kuwerenga mabukuwa.
Laibulale Yokwanira M’dzanja Limodzi
Pulogalamu ya JW Library yafotokozedwa kuti “ndi yamtengo wapatali kwambiri.” Onani zimene zimafunika kuti izikonzedwa komanso kusinthidwa.
Tchanelo cha JW Setilaiti Chimaoneka Kumene Kulibe Intaneti
Kodi abale a ku Africa amatani kuti aonere JW Broadcasting ngati alibe intaneti?
Kachipangizo Kothandiza Kwambiri
A Mboni za Yehova ambiri akutha kupanga dawunilodi mabuku ndi mavidiyo athu popanda kugwiritsa ntchito intaneti.
KUMANGA NDI KUKONZA
Kusamalira Nyumba za Ufumu
Padziko lonse tili ndi Nyumba za Ufumu zoposa 60,000. Kodi timasamalira bwanji nyumbazi?
Kuchita Zinthu Zothandiza Abale Athu Komanso Zosawononga Chilengedwe
Onani mmene tikugwiritsira ntchito zinthu zosawononga chilengedwe komanso mmene tachepetsera kugwiritsira ntchito zinthu monga malasha, mafuta komanso gasi.
Kuteteza Anthu pa Nyumba za Ufumu Panthawi ya COVID-19
Tinayambiranso kusonkhana pamasom’pamaso pa 1 April 2022. Werengani nkhaniyi kuti muone zimene zinachitika kuti abale ndi alongo akhale otetezeka akasonkhana m’Nyumba za Ufumu.
Maofesi a Omasulira Mabuku Omwe Akuthandiza Anthu Mamiliyoni
Dziwani mmene malo amene omasulira amagwirira ntchito yawo amakhudzira zimene akumasulira.
KUYENDETSA ZINTHU
Anateteza Ufulu wa Kulambira wa Anthu Akumidzi
Pamene anthu otsutsa anaphwanyira a Mboni za Yehova ufulu wawo wa kulambira, abale athu anawathandiza mwamsanga.
Zimene Ena Ali Nazo Zimathandizira pa Zimene Ena Akusowa
Kodi mayiko amene amapeza ndalama zochepa amathandizidwa bwanji kuti ntchito yathu iziyenda bwino?
KULALIKIRA NDI KUPHUNZITSA
Kuonera Kapena Kumvetsera Msonkhano
Msonkhano wachigawo wa chaka cha 2020 unaikidwa pa intaneti, koma anthu ambiri ku Malawi ndi ku Mozambique sangakwanitse kugwiritsa ntchito intaneti. Ndiye kodi anatha bwanji kumvetsera msonkhanowu?
Misonkhano Imene Anthu ‘Amamva ndi Kuona’
Onani zimene zimachitika kuti tizitha kumvetsera nkhani komanso kuonera mavidiyo pamisonkhano yathu.
Amishonale Amapita “Kumalekezero a Dziko Lapansi”
Kuli amishonale oposa 3,000 omwe akutumikira m’mayiko osiyanasiyana padziko lonse lapansi. Kodi amasamaliridwa bwanji?
Mmene Sukulu ya Giliyadi Imathandizira Padziko Lonse
Sukulu yofunika kwambiri imachitikira ku New York, koma ophunzira amachokera m’mayiko osiyanasiyana padziko lonse. Ndiye kodi ophunzirawa amayenda bwanji kuti akafike kusukuluyi?
Ntchito Yokonza Mavidiyo a Msonkhano Wachigawo wa 2020 Wakuti “Kondwerani Nthawi Zonse”
Kodi pamafunikanso zinthu ziti pokonza mavidiyo a misonkhano yathu yachigawo?
Ntchito Yomasulira Msonkhano Wachigawo wa 2020 Wakuti ‘Kondwerani Nthawi Zonse.’
Kodi n’chiyani chinathandiza kuti nkhani, masewero komanso nyimbo zimasuliridwe mofulumira kwambiri, m’zinenero zoposa 500?
Kuchita Misonkhano ya Mpingo pa Vidiyokomfelensi
Kodi gulu lathandiza bwanji mipingo kuti ikwanitse kumagwiritsa ntchito pulogalamu ya zoom yomwe ndi yotetezeka pochita misonkhano pa vidiyokomfelensi?
ZOKUGWA MWADZIDZIDZI
Sitinaiwale Abale ndi Alongo Athu Powathandiza Pangozi Zogwa Mwadzidzidzi mu 2021
M’chaka cha 2021, m’mayiko ena anthu ankafunika kuthandizidwa chifukwa cha mliri wa COVID-19 komanso ngozi zikuluzikulu zam’chilengedwe.
Kupereka Chithandizo Padziko Lonse pa Nthawi ya Mliri
Zimene tachita popereka chithandizo pa nthawi ya mliri wa COVID-19 zadabwitsa a Mboni komanso amene si Mboni.
Kuthandiza Anthu Amene Akhudzidwa Ndi Ngozi Zadzidzidzi
M’chaka chautumiki cha 2020, abale ndi alongo ambiri anakhudzidwa ndi mliri komanso ngozi zam’chilengedwe. Kodi tinawathandiza bwanji?
Pepani, palibe mawu ofanana ndi omwe mwasankha.

