Khalani Bwenzi la Yehova Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga! YAMBANI Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga! Dulani timapepalati tomwe mungaphunzirepo zinazake. Koperani Yam'mbuyo Yotsatira Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi KHALANI BWENZI LA YEHOVA—MAPHUNZIRO A MAVIDIYO Muzipemphera Nthawi Iliyonse Vidiyoyi ndi yoti mukhoza kuipanga dawunilodi ndipo imaphunzitsa ana nthawi komanso malo amene angapemphere kwa Yehova. KHALANI BWENZI LA YEHOVA—MAPHUNZIRO A MAVIDIYO Kuba N’koipa Kodi Mulungu amakuona bwanji kuba? Werengani Ekisodo 20:15. Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zambiri limodzi ndi Kalebe. KHALANI BWENZI LA YEHOVA—MAPHUNZIRO A MAVIDIYO Tiyeni Tikalalikire Kodi Sofiya watenga zonse zofunika popita kolalikira? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene inunso muyenera kutenga popita kolalikira. KHALANI BWENZI LA YEHOVA—MAPHUNZIRO A MAVIDIYO Uzipempha Mwaulemu Ndiponso Uzithokoza Kalebe waphunzira kuti kupempha mwaulemu ndiponso kuthokoza ndi kofunika kwambiri. KHALANI BWENZI LA YEHOVA—MAPHUNZIRO A MAVIDIYO Kupatsa N’kwabwino Pali zambiri zimene mungachite kuti muthandize ena. Kodi mukuganiza kuti mungachite chiyani? KHALANI BWENZI LA YEHOVA—MAPHUNZIRO A MAVIDIYO Uzikhala Waukhondo Yehova amaika chilichonse pamalo oyenera. Onani zimene nanunso mungachite kuti muzikhala aukhondo