Khalani Bwenzi la Yehova
Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga!
Dulani timapepalati tomwe mungaphunzirepo zinazake.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
Become Jehovah's Friend
Muzipemphera Nthawi Iliyonse
Vidiyoyi ndi yoti mukhoza kuipanga dawunilodi ndipo imaphunzitsa ana nthawi komanso malo amene angapemphere kwa Yehova.
Become Jehovah's Friend
Kuba N’koipa
Kodi Mulungu amakuona bwanji kuba? Werengani Ekisodo 20:15. Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zambiri limodzi ndi Kalebe.
Become Jehovah's Friend
Tiyeni Tikalalikire
Kodi Sofiya watenga zonse zofunika popita kolalikira? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene inunso muyenera kutenga popita kolalikira.
Become Jehovah's Friend
Uzipempha Mwaulemu Ndiponso Uzithokoza
Kalebe waphunzira kuti kupempha mwaulemu ndiponso kuthokoza ndi kofunika kwambiri.
Become Jehovah's Friend
Kupatsa N’kwabwino
Pali zambiri zimene mungachite kuti muthandize ena. Kodi mukuganiza kuti mungachite chiyani?
Become Jehovah's Friend
Uzikhala Waukhondo
Yehova amaika chilichonse pamalo oyenera. Onani zimene nanunso mungachite kuti muzikhala aukhondo
ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA