Khalani Bwenzi la Yehova
Ndakonzekera Kuchita Zambiri
Tikakhala ndi zolinga zauzimu Yehova amaona kuti timaganizira kwambiri za iyeyo. Kodi iweyo uli ndi zolinga zotani?
Khalani Bwenzi la Yehova
Tikakhala ndi zolinga zauzimu Yehova amaona kuti timaganizira kwambiri za iyeyo. Kodi iweyo uli ndi zolinga zotani?