KHALANI BWENZI LA YEHOVA​—ZOCHITA

Munachitira Ine Amene

Chichewa
Munachitira Ine Amene
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/501700056/univ/art/501700056_univ_sqr_xl.jpg

Khalani Bwenzi la Yehova

Munachitira Ine Amene

Munachitira Ine Amene

Tingathandize Akhristu odzodzedwa m’njira zambiri. Tiyeni tione zina mwa njirazi.

Makolo, werengani n’kukambirana ndi ana anu lemba la Mateyu 25:40.

Pangani dawunilodi n’kupulinta.

Mukaonera vidiyo yakuti, Munachitira Ine Amene, kambiranani ndi ana anu njira zosiyanasiyana zolalikirira, zakale ndi zamasiku ano zomwe, ndipo musankhepo njira imodzi yoti muifufuze pamodzi.