Khalani Bwenzi la Yehova
Lowezani Salimo 133:1
Mukaimba nyimbo nambala 20, kongoletsani tsambali ndi chekeni. Kenako lowezani lemba la Salimo 133:1, kuti likuthandizeni kukumbukira zoti misonkhano yathu ndi yofunika kwambiri.


KHALANI BWENZI LA YEHOVA—ZOCHITA
Khalani Bwenzi la Yehova
Mukaimba nyimbo nambala 20, kongoletsani tsambali ndi chekeni. Kenako lowezani lemba la Salimo 133:1, kuti likuthandizeni kukumbukira zoti misonkhano yathu ndi yofunika kwambiri.