Khalani Bwenzi la Yehova​—Zochita

Izi ndi zochita zosiyanasiyana zomwe zaikidwa pamodzi pofuna kuti muzisangalala ndi ana anu.

Thandizani Kalebe Kukonza M’nyumba

Pangani dawunilodi kapena sindikizani tsambali ndipo muthandizeni Kalebe kupeza zidole zake 5 zomwe akufunika kuchotsa m’nyumba.

Muzipemphera Nthawi Iliyonse: Nyimbo ndi Mawu Ake

Pangani dawunilodi mawu a nyimbo yomwe mungathe kusindikiza. Ana adzaikonda nyimbo yosavuta kuphunzirayi.

Kodi Kalebe Akuwerenga Buku Lanji?

Onerani vidiyo yakuti, “Kuba N’koipa.” Kenako sindikizani tsambali ndipo mulikongoletse ndi chekeni.

Pangani Chikwama cha mu Utumiki

Kodi mumafunika kutenga chiyani popita kolalikira? Tsambali lingakuthandizeni kuti muzitenga chikwama popita mu utumiki.

Kukonzekera Kupita Kolalikira

Kodi mungasankhe zovala zimene Kalebe ndi Sofiya akufunika kuvala pokalalikira?

Panga Galimoto ya Kalebe

Sindikiza, dula ndi kulumikiza galimoto ya Kalebe.

Lowezani Salimo 83:18

N’chifukwa chiyani Yehova amatchedwa kuti “Wam’mwambamwamba wolamulira dziko lonse lapansi”?

Kodi Uyenera Kuchita Chiyani?

Onerani vidiyo yakuti “Uzikhululuka ndi Mtima Wonse” kenako sindikizani tsambali ndipo mukongoletse chithunzi cholondola.

Lowezani Salimo 133:1

Tikasonkhana, Yehova amatidalitsa potithandiza kuti tikhale ogwirizana komanso a mtendere.

Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga!

Mungagwiritsire ntchito timapepalati kudziwa malo omwe mumawerenga m’mabuku anu!

Kodi Zithunzizi Zikusiyana Pati?: Zochita Zokhudza Misonkhano

Yerekezerani zithunzizi. Kodi chingakuthandizeni ndi chiyani kuti muzimvetsera kwambiri nthawi ya misonkhano?

Kodi Yehova Angakuthandize Bwanji Kuti Ukhale Wolimba Mtima?

Yehova angakuthandize ngati mmene anathandizira kamtsikana ka ku Isiraeli.

Kuyerekezera: Moyo Wapanopa ndi Wam’tsogolo

Kodi ndi malonjezo ati a m’Baibulo omwe adzakwaniritsidwe m’Paradaiso?

Thandizani Anthu Ambiri Pogwiritsa Ntchito Pulogalamu Yothandiza Kuphunzira Chinenero pa JW

Phunzirani mawu a m’chinenero china kuti muzithandiza anthu kuphunzira zokhudza Yehova.

Muzikonda Anthu Onse

Kodi Yehova amasonyeza bwanji kuti amakonda anthu onse?

Lowezani Mabuku a M’Baibulo (Gawo 1)

Gwiritsani ntchito makadi a mabuku a m’Baibulo kuti akuthandizeni kuloweza mabuku a Chiheberi, kuyambira Genesis mpaka Yesaya.

Lowezani Mabuku a M’Baibulo (Gawo 2)

Gwiritsani ntchito makadiwa kuti akuthandizeni kuloweza mabuku a Malemba a Chiheberi, kuyambira Yeremiya mpaka Malaki.

Kunena Zoona Kuli Ngati Kumanga Mlatho

N’chifukwa chiyani kunena zoona kungathandize kuti muzigwirizana kwambiri ndi anzanu?

Kodi Ungatani Kuti Ukhale Woleza Mtima?

Kodi ndi njira zina ziti zimene ungasonyezere kuti ndiwe woleza mtima?

Dongosolo la Banja Limene Yehova Anakhazikitsa

Kodi m’Baibulo mungapezemo mabanja a ndani?

Imbirani Yehova Nyimbo

Dulani zithunzizi ndi kuziika malo amodzi potsatira malangizo ndipo kenako imbirani Yehova komanso loweza nyimbo ya mutu wakuti “Dzina Lanu Ndinu Yehova.”

Dzina la Yehova

Kodi dzina la Mulungu limapezeka maulendo angati m’Baibulo?

Yehova Anapanga Zinthu Zokongola

Kodi ndi zinthu zingati zimene Yehova analenga zomwe mungathe kuzipeza m’chithunzicho?

Tizilalikira kwa Anthu a Mitundu Yonse

Kodi uthenga wa Ufumu uyenera kulalikidwa kwa ndani?

Pezani Anzanu Enieni

N’chifukwa chiyani ndi bwino kukhala ndi anzanu omwe ndi achikulire?

Lolani Kuti Yehova Akuphunzitseni

Mulungu angakuphunzitseni kuti mukhale olimba ndiponso amphamvu.

Tchati Chosonyeza Moyo wa Yesu

Werengani malemba a m’Baibulo ndipo agwirizanitseni ndi chithunzi chogwirizana ndi lemba lililonse.

Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi

Kodi ndi zinthu ziti zimene mungachite zomwe zingakuthandizeni kuti muzikonda kwambiri choonadi?

Mmene Tingasonyezere Chikondi Kwa Ena

Kodi tingatsanzire bwanji Yesu pa nkhani yosonyeza ena chikondi?

Yerekezera Kuti Uli M’Paradaiso

Kodi ndi chinthu chiti chimene ukuchiyembekezera kwambiri m’Paradaiso?

Uzipilira Ena Akakuchitira Nkhanza

Kodi tizitani ena akatichitira zinthu zankhanza?

Kuphunzira za Mabwenzi a Yehova

Gwiritsani ntchito zoti muchitezi kuti muyambe kuphunzira Baibulo panokha.

Uzidzichepetsa

Phunzirani zokhudza kudzichepetsa kuchokera kwa anthu osiyanasiyana otchulidwa m’Baibulo.

Tili ndi Zifukwa Zambiri Zokhalira Osangalala

Kodi ndi nyama iti yomwe ukufunitsitsa kudzasewera nayo m’dziko latsopano la Mulungu?

Kupilira Imfa ya Munthu Yemwe Munkamukonda

Kodi n’chiyani chomwe chingatithandize kukhalabe osangalala pamene munthu yemwe tinkamukonda wamwalira?

Kunyumba ndi Nyumba

Kodi ndi zinthu ziti zomwe ukufuna kugwiritsa ntchito muutumiki?

Uzipempherera Ena

Kodi ndi anthu ati omwe ungawapempherere?

Uzikonda Nyumba ya Yehova

Uziyesetsa kuchita zinthu zomwe zingathandize kuti nyumba ya Mulungu izikhala yoyera nthawi zonse

Ndakonzekera Kuchita Zambiri

Yehova amafuna kuti tizikhala ndi zolinga zauzimu. Kodi iweyo uli ndi zolinga zotani?

Lambirani Yehova Mudakali Achinyamata

Mungasonyeze bwanji kuti ndinu oyamikira?

Yehova ndi Mnzanga Wapamtima

Mulungu analenga zomera ndiponso zinyama kuti anthufe tizisangalala chifukwa chakuti iye ndi Mnzathu

Uzichita Zinthu Bwino Muutumiki

Mungatani kuti muchita zinthu zabwino muutumiki?

Muzikhululuka

N’chiyani chingakuthandizeni kuti muzikhululukira ena?

Nyimbo Yofotokoza Mavidiyo ndi Zinthu Zina za Khalani Bwenzi la Yehova

Kodi ukukumbukira zina mwa zinthu zimene Kalebe ndi Sofiya aphunzira m’Baibulo?

“Ndikufuna”

Yesu amakonda kuthandiza ena. Ungatani kuti nawenso uzichita ngati Yesu?

Timakonda Kulambira kwa Pabanja

Kodi banja lanu lingachite zotani kuti muzisangalala kwambiri ndi kulambira kwa pabanja?

Muzigwiritsa Ntchito Nthawi Mwanzeru

Kodi lemba la Aefeso 5:15, 16 lingakuthandizeni bwanji kugwiritsa ntchito nthawi mwanzeru?

Ntchito Zodabwitsa za Mulungu

Kodi ungatchule nyama zingati?

Ili ndi Banja Lathu

Dziwani zokhudza banja lanu!

Kodi Mumamva Bwanji?

Kodi ungatani kuti uzilalikira mwakhama?

Zikomo Kuti Ndinu Mnzanga

Anzathu enieni amatithandiza kuti tizikonda Yehova.

Uzikhala Wokhulupirika

Yehova amakonda anthu okhulupirika.

Uzikonda Mnzako

Kodi Sofiya angasonyeze bwanji chikondi ndiponso kukoma mtima?

Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha

Kodi Yehova anasonyeza bwanji kuti iye ndi amene anayamba kutikonda?

Uzipirira Ngati Nowa

Phunzirani zimene mungachite kuti muzipirira ngati mmene Nowa anachitira.

Esitere Anali Wolimba Mtima

Phunzira zimene ungachite kuti ukhale wolimba mtima ngati Esitere.

Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano

Kodi mungadziyerekezere muli m’dziko latsopano?

Chikondi cha Mulungu

Tingasonyeze bwanji kuti timakonda ena ngati mene Yehova amachitira?

Yehova Amakhululuka

Yehova amakhala wokonzeka kutikhululukira nthawi zonse.

Kodi Tiyenera Kukondwerera Mabefide?

Onani chifukwa chake sitikondwerera mabefide.

Buku la Mulungu Ndi Chuma

Baibulo ndi mphatso yochokera kwa Yehova.

Mariya​—Anali Wodzichepetsa ndi Wololera

Mofanana ndi Mariya, nafenso tingathe kukhalabe okhulupirika kwa Yehova kaya tikumane ndi zotani.

Tipitirizabe Kupirira

Tingathe kupirira mavuto tikamaganizira zinthu zabwino zomwe tikuyembekezera m’tsogolo.

Rute Anali Bwenzi Lenileni

Ungafanane ndi Rute pokhala bwenzi lenileni.

Davide Ndi Chitsanzo Chabwino kwa Ana

Davide ali mnyamata anayamba kukhala pa ubwenzi wolimba ndi Yehova ndipo ubwenziwo unkamuthandiza pa moyo wake wonse.

Kodi Yehova Amayankha Mapemphero?

Nthawi zina Yehova amayankha mapemphero m’njira yomwe sitinkayembekezera.

Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse

Timafunika kuchita khama kuti tikhale pa ubwenzi wolimba ndi Yehova, koma kuchita zimenezi n’kothandiza kwambiri

Munachitira Ine Amene

Atumiki a Yehova amasangalala kuchita chilichonse pofuna kuthandiza odzodzedwa.

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kumvera Mulungu Ngakhale Sitimamuona?

Onani zinthu zokongola zimene Mulungu analenga. Zimatithandiza kukumbukira kuti iye aliko ngakhale kuti sitingathe kumuona.

Fufuzani Anthu Oyenerera

Kufufuza anthu oyenerera si kutaya nthawi.

Uzisangalatsa Yehova

Mukhoza kumachita zinthu zoyenera n’kusangalatsa Yehova.