Khalani Bwenzi la Yehova
Onani kapena tsitsani mavidiyo ojambula omwe amaphunzitsa ana maphunziro ofunika a Baibulo.
Ukhoza Kuchita Upainiya
Kalebe akuganiza zochita upainiya pambuyo pomva zimene zalengezedwa ku Nyumba ya Ufumu.
Anasonyeza Chikondi Chachikulu Kwambiri
Dziwani chifukwa chake nsembe ndi mphatso yapadera kwambiri imene anthu anapatsidwa.
Zomwe Zili Muvidiyo ya Khalani Bwenzi la Yehova: Yehova Amakuona Kuti Ndiwe Wofunika
Zowe waphunzira kuti kukhala osiyana ndi ena kukhoza kukhala kwabwino.
Ukhale Wofalitsa Wosabatizidwa
Kalebe akuphunzira zimene angachite kuti akhale wofalitsa wosabatizidwa.
Phunziro 47: Ndi Ndani Angakhale Mnzanga?
Yehova amafuna kuti ukhale ndi anzako, koma kodi ungasankhe bwanji anzako abwino?
Phunziro 45: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kumvera Mulungu Ngakhale Sitimamuona?
Ngakhale kuti sitingathe kuona Mulungu, nanga n’chifukwa chiyani timamumvera? Tiyeni tione mmene Sofiya akuyankhira funso limeneli.
Zimene Zili Muvidiyo ya Khalani Bwenzi la Yehova: Kodi Yehova Amayankha Mapemphero?
Onani mmene Yehova akuyankhira mapemphero a Sofiya.
Phunziro 41: Kodi Tiyenera Kukondwerera Mabefide?
Kodi ungathandize bwanji anthu ena kumvetsa chfukwa chake sumakondwerera mabefide?
Phunziro 40: Yehova Amakhululuka
Tikalakwitsa chinachake, kodi tizinyanyala? Tiyeni tione zimene Kalebe waphunzira m’nkhani inayake ya m’Baibulo.
Phunziro 38: Uzikonda Mnzako
Kodi ungatengere bwanji chitsanzo cha Msamariya wachifundo posonyeza chikondi kwa anzako?
Phunziro 37: Kudzimana
Yesu ankadzimana nthawi zonse n’cholinga choti athandize ena. Kodi ungamutsanzire bwanji Yesu?
Phunziro 36: Amatilangiza Chifukwa Chotikonda
N’chifukwa chiyani Yehova amalangiza amene amawakonda?
Phunziro 35: Muzigwiritsa Ntchito Nthawi Mwanzeru
Nthawi ndi mphatso yochokera kwa Yehova. Muziigwiritsa ntchito mwanzeru.
Phunziro 33: Uzisangalatsa Yehova
Zimene mumachita tsiku lililonse zingasangalatse mtima wa Mulungu.
Phunziro 32: Uzichita Zinthu Bwino Muutumiki
Usanapite muutumiki, pali zinthu zitatu zimene uyenera kuzidziwa.
Phunziro 31: Uzikonda Nyumba ya Yehova
Kodi mumagwira nawo ntchito yoyeretsa Nyumba ya Ufumu?
Phunziro 30: Kupirira Imfa ya Munthu Yemwe Munkamukonda
N’chiyani chingatithandize kuti tipirire imfa ya munthu yemwe tinkamukonda?
Phunziro 29: Uzidzichepetsa
Kalebe anazindikira tanthauzo la kukhala wodzichepetsa.
Phunziro 27: Yerekezera Kuti Uli M’Paradaiso
Kodi umadziyerekezera uli m’dziko latsopano?
Phunziro 26: Dipo
Kodi dipo lingatithandize bwanji tikakumana ndi mavuto panopa?
Phunziro 25: Mmene Mungapezere Anzanu
Kodi ndi ndani angakhale mnzanu mumpingo?
Phunziro 24: Yehova Anapanga Zinthu Zonse Modabwitsa
Mulungu anapanga zinthu zambiri zodabwitsa. Kodi inu mumakonda chiyani?
Phunziro 23: Dzina la Yehova
Kodi umadziwa zimene dzina la Mulungu limatanthauza?
Phunziro 22: Mwamuna Mmodzi, Mkazi Mmodzi
Kodi Mulungu anapereka mfundo zotani zokhudza ukwati nanga n’chifukwa chiyani tiyenera kuzitsatira?
Phunziro 21: Ukhoza Kukhala Woleza Mtima
Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene zinamuthandiza Kalebe kuti akhale woleza mtima.
Phunziro 20: Uzinena Zoona
N’chifukwa chiyani nthawi zonse uyenera kunena zoona?
Phunziro 19: Uzikhala Wopatsa
Kodi ndi zinthu zabwino ziti zimene zimachitika chifukwa chakuti atumiki a Yehova ndi wopatsa?
Phunziro 18: Uzilemekeza Nyumba ya Yehova
Kodi mungasonyeze bwanji khalidwe labwino ku nyumba imene timalambiriramo Yehova?
Phunziro 17: Tetezani Ana Anu
Kalebe ndi sofiya akuphunzira zimene angachite kuti akhale otetezeka.
Phunziro 16: Muzilalikira Anthu Olankhula Chinenero cha Dziko Lina
Kodi mungatani kuti mulalikire munthu amene samatha kulankhula chinenero chanu?
Phunziro 15: Muzimvetsera Tikakhala Pamisonkhano
N’chifukwa chiyani tiyenera kumvetsera tikakhala pamisonkhano?
Phunziro 14: Uzikonzekera Zimene Ukayankhe
Kodi ndi zinthu 4 ziti zimene mungachite pokonzekera zimene mukayankhe kumisonkhano?
Phunziro 13: Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima
N’chiyani chingakuthandizeni kuti muziuza ena zokhudza Yehova molimba mtima?
Phunziro 12: Kalebe ndi Sofiya Akukaona Malo ku Beteli
Onani Kalebe ndi Sofiya akuona zithunzi ku Beteli. Muonanso ntchito imene imachitika ku Beteli.
Mavidiyo Amakatuni Omwe Ana Akuwakonda Kwambiri
A Mboni za Yehova akupanga mavidiyo amakatuni pofuna kuphunzitsa ana mmene angagwiritsire ntchito mfundo za m’Baibulo. Onani zimene zimachitika pokonzekera mavidiyowa kuti mudziwe mmene amawapangira.
Phunziro 11: Uzikhululuka ndi Mtima Wonse
Kodi munthu akakuchitirani choipa muyenera kumutani?
Phunziro 10: Uzikhala Wokoma Mtima Ndiponso Wopatsa
Onerani kuti mudziwe mmene Kalebe ndi Sofiya amasangalalira akamagawana zinthu.
Phunziro 9: “Yehova . . . Analenga Zinthu Zonse”
Kodi ukudziwa zinthu zimene Mulungu anayambirira kulenga? Onera vidiyoyi kuti udziwe mmene Mulungu analengera zinthu zosiyanasiyana.
Phunziro 8: Uzikhala Waukhondo
Yehova amaika chilichonse pamalo oyenera. Onani zimene nanunso mungachite kuti muzikhala aukhondo
Phunziro 7: Kupatsa N’kwabwino
Pali zambiri zimene mungachite kuti muthandize ena. Kodi mukuganiza kuti mungachite chiyani?
Phunziro 6: Uzipempha Mwaulemu Ndiponso Uzithokoza
Kalebe waphunzira kuti kupempha mwaulemu ndiponso kuthokoza ndi kofunika kwambiri.
Phunziro 5: Tiyeni Tikalalikire
Kodi Sofiya watenga zonse zofunika popita kolalikira? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene inunso muyenera kutenga popita kolalikira.
Phunziro 4: Kuba N’koipa
Kodi Mulungu amakuona bwanji kuba? Werengani Ekisodo 20:15. Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zambiri limodzi ndi Kalebe.
Phunziro 3: Muzipemphera Nthawi Iliyonse
Vidiyoyi ndi yoti mukhoza kuipanga dawunilodi ndipo imaphunzitsa ana nthawi komanso malo amene angapemphere kwa Yehova.
Phunziro 2: Muzimvera Yehova
Kodi matoyi amene mumaseweretsa angakhale ndi vuto? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene Kalebe anachita kuti akhale bwenzi la Yehova
Phunziro 1: Muzimvera Makolo Anu
N’chifukwa chiyani kumvera makolo anu kuli kofunika? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe chifukwa chake limodzi ndi Kalebe.
Pepani, palibe mawu ofanana ndi omwe mwasankha.

