N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa? YAMBANI N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa? Baibulo limasonyeza kuti imfa ya Yesu ndi yofunika kwambiri. Komano kodi imfa yake ili ndi phindu lililonse? Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Yam'mbuyo Yotsatira Nkhani Zina Mavidiyo Othandiza Kumvetsa Mfundo Zofunika za M’baibulo Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBULO N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa? Anthu ambiri amadziwa mfundo yakuti Yesu anafa ndi cholinga choti tikhale ndi moyo. Koma kodi imfa ya Yesu imatithandiza bwanji kwenikweni? KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBULO Kodi Yesu Amatipulumutsa Bwanji? N’chifukwa chiyani Yesu amafunika kuchonderera m’malo mwathu? Kodi kungokhulupirira Yesu n’kokwanira kuti tidzapulumuke? MFUNDO ZOFUNIKA ZA M'BAIBULO Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani? Ali padziko lapansi, Yesu anafotokoza kwambiri za Ufumu wa Mulungu kuposa nkhani ina iliyonse. Kwa zaka zambiri otsatira ake akhala akupempherera Ufumu umenewu kuti ubwere. KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBULO Kodi Nsembe ya Yesu Imawombola Bwanji “Anthu Ambiri”? Kodi dipo limawombola bwanji anthu ku uchimo? ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA Yambani Kuphunzira Baibulo Phunzirani Baibulo kwaulere, mochita kukambirana ndi mphunzitsi wanu. ZOKHUDZA IFEYO Mwambo Wokumbukira Imfa ya Yesu A Mboni za Yehova akukuitanirani ku Mwambo Wokumbukira Imfa ya Yesu womwe udzachitike pa 2 April 2026. Sindikizani Patsani ena Patsani ena N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa? MFUNDO ZOFUNIKA ZA M'BAIBULO N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa? Chichewa N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa? https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/502016853/univ/art/502016853_univ_sqr_xl.jpg