MFUNDO ZOFUNIKA ZA M'BAIBULO

N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa?

Chichewa
N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa?
https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/502016853/univ/art/502016853_univ_sqr_xl.jpg

N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa?

N’chifukwa Chiyani Yesu Anafa?

Baibulo limasonyeza kuti imfa ya Yesu ndi yofunika kwambiri. Komano kodi imfa yake ili ndi phindu lililonse?