NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA) November 2023
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira January 8–February 4, 2024.
NKHANI YOPHUNZIRA 46
Mmene Yehova Anatsimikizira Lonjezo Lake la Paradaiso
Idzaphunziridwa mlungu woyambira January 8-14, 2024.
NKHANI YOPHUNZIRA 47
Kodi Tingatani Kuti Tizikondana Kwambiri?
Idzaphunziridwa mlungu woyambira January 15-21, 2024.
NKHANI YOPHUNZIRA 48
Mukhoza Kukhalabe Olimba Mtima pa Nthawi Yovuta
Idzaphunziridwa mlungu woyambira January 22-28, 2024.
NKHANI YOPHUNZIRA 49
Kodi Yehova Amayankha Mapemphero Anga?
Idzaphunziridwa mlungu woyambira January 29–February 4, 2024.
MBIRI YA MOYO WANGA
Ndimakhala Wosatekeseka Chifukwa Chodalira Yehova
Mbiri ya moyo wanga: Israel Itajobi.
Hulda Anakwaniritsa Cholinga Chake
Kodi Hulda anatani kuti apeze tabuleti yoti izimuthandiza mu utumiki komanso pamisonkhano?

