GALAMUKANI! Na. 4 2016 | Kodi N’zotheka Kusintha Zomwe Munazolowera?
Zinthu zimene tinazolowera zingatithandize kapena kutibweretsera mavuto, ndipo nthawi zina zimenezi zingachitike tisakudziwa n’komwe.
NKHANI YAPACHIKUTO
Kodi N’zotheka Kusintha Zomwe Munazolowera?
Muzizolowera kuchita zinthu zabwino osati zoipa.
NKHANI YAPACHIKUTO
1 N’zosatheka Kusintha Lero ndi Lero
N’zosatheka kusiya zoipa zomwe munazolowera n’kuyamba zabwino lero ndi lero. Onani zomwe zingakuthandizeni.
NKHANI YAPACHIKUTO
2 Muzichita Zinthu Zomwe Zingakuthandizeni Kukwaniritsa Zolinga Zanu
Muzikhala malo komanso kucheza ndi anthu omwe angakuthandizeni kuti muzichita zinthu zabwino.
NKHANI YAPACHIKUTO
3 Musafulumire Kugwa Ulesi
Ngakhale zitamakuvutani kusiya zinthu zomwe munazolowera kapena kuzolowera zinthu zatsopano, musagwe ulesi.
Kodi Baibulo Limalola kuti Akazi Kapena Amuna Okhaokha Azigonana?
Kodi Baibulo limaletsa kugonana kwa amuna kapena akazi okhaokha? Kodi limalimbikitsa anthu kuti azidana ndi amuna kapena akazi ogonana okhaokha?
MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA
Zimene Mungachite Zinthu Zikasintha
Zinthu zimasintha pamoyo. Onani zimene ena achita kuti azolowere zinthu zitawasinthira.
ANTHU NDI MAYIKO
Dziko la Kyrgyzstan
Anthu a ku Kyrgyzstan ndi ochereza komanso aulemu. Kodi amatsatira miyambo yanji yokhudza banja?
ZIMENE BAIBULO LIMANENA
Kukongola
Makampani ofalitsa nkhani komanso opanga zovala angapangitse anthu kuti azingoganizira za maonekedwe awo.
KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?
Nyenje za Moyo Wautali
Nyenjezi ndi zodabwitsa kwambiri chifukwa zimaonekera kunja kwa milungu yochepa yokha pambuyo pa zaka 13 kapena 17.
Zina zimene zili pawebusaiti
Zimene Mungachite Kuti Musamakangane
Kodi simuchedwa kukangana ndi mwamuna kapena mkazi wanu? Werengani nkhaniyi kuti mudziwe mfundo zimene zingathandize banja lanu.
Achinyamata Ena Akufotokoza Zokhudza Kukhulupirira Kuti Kuli Mulungu
M’vidiyo ya maminitsi atatuyi, achinyamata akufotokoza chifukwa chake amakhulupirira kuti kuli Mulungu.